Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 20:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Jonatani ananena kwa Davide, Muka mumtendere, popeza tonsefe tinalumbira m'dzina la Yehova, kuti, Yehova adzakhala pakati pa ine ndi iwe, ndi pakati pa mbeu yanga ndi mbeu yako, nthawi zamuyaya.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 20

Onani 1 Samueli 20:42 nkhani