Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 19:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiponso anabvula zobvala zace, naneneranso pamaso pa Samueli nagona wamarisece usana womwe wonse, ndi usiku womwe wonse. Cifukwa cace amati, Kodi Saulinso ali pakati pa aneneri?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 19

Onani 1 Samueli 19:24 nkhani