Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 19:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapita komweko ku Nayoti m'Rama; ndi mzimu wa Mulungu unamgwera iyenso; ndipo anapitirira, nanenera, mpaka anafika ku Nayoti m'Rama.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 19

Onani 1 Samueli 19:23 nkhani