Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 19:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo iyenso anamuka ku Rama, nafika ku citsime cacikuru ciri ku Seku, nafunsa Dati, Samueli ndi Davide ali kuti? Ndipo wina anati, Taonani, ali ku Nayoti m'Rama.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 19

Onani 1 Samueli 19:22 nkhani