Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:56-58 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

56. Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani.

57. Ndipo pamene Davide anabwera, atapha Mfilistiyo, Abineri anamtenga, nafika naye pamaso pa Sauli, mutu wa Mfilistiyo uli m'dzanja lace.

58. Ndipo Sauli anati kwa iye, Mnyamata iwe, ndiwe mwana wa yani? Davide nayankha, Ndiri mwana wa kapolo wanu Jese wa ku Betelehemu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17