Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 17:55 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene Sauli anaona Davide alikuturukira kwa Mfilistiyo, iye anati kwa Abineri, kazembe wa khamu la nkhondo, Abineri, mnyamata uyu ndi mwana wa yani? Nati Abineri, Pali moyo wanu, mfumu, ngati ndidziwa.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 17

Onani 1 Samueli 17:55 nkhani