Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 13:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Aisrayeli onse anamva kunena kuti Sauli anathyola kaboma ka Afilisti, ndi kuti Afilisti anyansidwa ndi Aisrayeli. Ndipo anthuwo anasonkhana kwa Sauli ku Giligala.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 13

Onani 1 Samueli 13:4 nkhani