Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 12:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mukapanda kumvera mau a Yehova, ndi kupikisana ndi lamulo la Yehova, dzanja la Yehova lidzatsutsana nanu, monga linatsutsana ndi makolo anu.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12

Onani 1 Samueli 12:15 nkhani