Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 1:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Hana sadakwera, cifukwa kuti anati kwa mwamuna wace, Sindidzakwerako kufikira mwanayo ataleka kuyamwa, pamenepo ndidzapita naye kuti aoneke pamaso pa Yehova, ndi kukhalako cikhalire.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 1

Onani 1 Samueli 1:22 nkhani