Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 9:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo caka cimodzi Solomo anapereka katatu nsembe zopsereza ndi zamtendere, pa guwa la nsembe limene anammangira Yehova, nafukiza zonunkhira pa guwa la nsembe pamaso pa Yehova, atatsiriza nyumbayo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 9

Onani 1 Mafumu 9:25 nkhani