Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 8:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo akakumbukila mitima yao, ali kudziko kumene anatengedwa ukapolo, nakalapa, nakapembedza inu m'dziko la iwo anawatenga ndende, ndi kuti, Tacimwa, ndipo tacita mphulupulu, tacita moipa;

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:47 nkhani