Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 8:46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akacimwira Inu, popeza palibe munthu wosacimwa, ndipo mukakwiya nao ndi kuwapereka kwa adani, kuti iwo awatenge ndende kumka nao ku dziko la adani, ngati kutali kapena kufupi,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:46 nkhani