Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Izi zonse zinali za miyala ya mtengo wapatali yosemasema, ya muyeso muyeso, yoceka ndi mipeni ya mano mana m'katimo ndi kunjako, kuyambira kumazikokufikira kumutu, momwemonso kunjako ku bwalo lalikuru,

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:9 nkhani