Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo nyumba yace yakukhalamo iye, m'bwalo lina la m'tsogolo mwa khumbilo, linamangidwa cimodzimodzi. Anammangiranso nyumba mwana wamkazi wa Farao, amene adamkwatira Solomo, yofanafana ndi khumbi limeneli.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:8 nkhani