Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaika maphaka asanu ku dzanja lamanja la nyumba, ndi maphaka asanu ku dzanja lamanzere la nyumba; naika thawalelo ku dzanja lamanja la nyumba kum'mawa kupenya kumwera.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:39 nkhani