Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapanga mitu iwiri ya mkuwa wosungunula, kulika pamwamba pa nsanamirazo, msinkhu wace wa mutu wina unali mikono isanu, ndi msinkhu wa mutu unzace mikono isanu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:16 nkhani