Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 7:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali maukonde olukaluka ndi zoyangayanga, zokolana za pa mitu imene inali pamwamba pa nsanamira; zisanu ndi ziwiri za pa mutu wina, ndi zisanu ndi ziwiri za pa mutu unzace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 7

Onani 1 Mafumu 7:17 nkhani