Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 6:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo nyumbayo pomangidwa inamangidwa ndi miyala yokonzeratu asanaitute; ndipo m'nyumbamo simunamveka: kulira nyundo, kapena nkhwangwa, kapena cipangizo cacitsulo, pomangidwa iyo.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 6

Onani 1 Mafumu 6:7 nkhani