Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 6:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo nyumbayo mfumu Solomo anaimangira Yehova, m'litali mwace munali mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi m'mimba mwace mikono makumi awiri, ndi msinkhu wace mikono makumi atatu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 6

Onani 1 Mafumu 6:2 nkhani