Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 6:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamanga likole pakhomo pa nyumba ya kacisiyo, m'litali mwace munali mikono makumi awiri monga m'mimba mwace mwa nyumbayo, kupingasa kwace kunali mikono khumi ku khomo la nyumba.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 6

Onani 1 Mafumu 6:3 nkhani