Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 21:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, atamva Yezebeli kuti anamponya Naboti miyala nafa, Yezebeli anati kwa Ahabu, Taukani, landirani munda wamphesa wa Naboti Myezreeli uja anakana kukugulitsani ndi ndarama, popeza, Naboti sali ndi moyo, koma wafa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 21

Onani 1 Mafumu 21:15 nkhani