Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 21:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo zitatha izi, kunaoneka zotere: Naboti wa ku Yezreeli anali ndi munda wamphesa, unali m'Yezreelimo, m'mbali mwa nyumba ya Ahabu mfumu ya ku Samaria.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 21

Onani 1 Mafumu 21:1 nkhani