Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 18:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Ahabu anati kwa Obadiya, Kayendere dziko lonse ku zitsime zonse zamadzi, ndi ku mitsinje yonse, kapena tikapeza msipu ndi kusunga moyo wa akavalo ndi nyuru, zingafe nyama zonse.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 18

Onani 1 Mafumu 18:5 nkhani