Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 18:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo anatenga ng'ombe ija adawapatsa, naikonza, naitana dzina la Baala, kuyambira m'mawa kufikira pausana, nati, Baala, timvereni ife. Koma panalibe mau kapena wobvomereza. Ndipo anabvinabvina kuguwa adalimanga.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 18

Onani 1 Mafumu 18:26 nkhani