Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzamninkha mwana wace pfuko limodzi, kuti Davide mtumiki wanga akhale cikhalire ndi nyali pamaso panga m'Yerusalemu, mudzi umene ndinadzisankhira kuikapo dzina langa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:36 nkhani