Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 11:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anacoka ku Midyani nafika ku Parani, natenga anthu a ku Parani pamodzi nao, nafika ku Aigupto kwa Farao mfumu ya Aigupto, ameneyo anampatsa nyumba, namnenera zakudya, nampatsako dziko.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 11

Onani 1 Mafumu 11:18 nkhani