Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 10:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo gareta limodzi linacokera kuturuka m'Aigupto mtengo wace masekeli a siliva mazana asanu ndi limodzi, ndi kavalo mtengo wace masekeli zana limodzi mphambu makumi asanu; momwemonso iwo anawagulira mafumu onse a Ahiti ndi mafumu a Aramu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 10

Onani 1 Mafumu 10:29 nkhani