Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 5:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Ine ndiri nao umboni woposa wa Yohane; pakuti nchito zimene Atateanandipatsa ndizitsirize, nchito zomwezo ndizicita zindicitira umboni, kuti Atate anandituma Ine.

Werengani mutu wathunthu Yohane 5

Onani Yohane 5:36 nkhani