Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 19:34-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. koma mmodzi wa asilikari anamgwaza ndi nthungo m'nthiti yace, ndipo 2 panaturuka pomwepo mwazi ndi madzi.

35. Ndipo 3 iye amene anaona, wacita umboni, ndi umboni wace uti woona; ndipo iyeyu adziwa kuti anena zoona, kuti inunso mukakhulupire.

36. Pakuti izi zinacitika, kuti lembo likwaniridwe, 4 Pfupa la iye silidzatyoledwa.

37. Ndipo linenanso lembo lina, 5 Adzayang'ana pa iye amene anampyoza.

Werengani mutu wathunthu Yohane 19