Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yohane 15:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene wafika Nkhoswe, amene Ine ndidzamtuma kwa inu kucokera kwa Atate, ndiye Mzimu wa coonadi, amene aturuka kwa Atate, Iyeyu adzandicitira Ine umboni.

Werengani mutu wathunthu Yohane 15

Onani Yohane 15:26 nkhani