Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yakobo 1:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iye wakupenyerera m'lamulo langwiro, ndilo laufulu, natero cipenyerere, ameneyo, posakhala wakumva wakuiwala, komatu wakucita nchito, adzakhala wodala m'kucita kwace.

Werengani mutu wathunthu Yakobo 1

Onani Yakobo 1:25 nkhani