Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mateyu 21:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndani wa awiriwo anacita cifuniro ca atate wace? Iwo ananena, Woyambayo. Yesu ananena kwa iwo, Indetu ndinena kwa inu, kuti amisonkho ndi akazi aciwerewere amatsogolera inu, kulowa mu Ufumu wa Kumwamba.

Werengani mutu wathunthu Mateyu 21

Onani Mateyu 21:31 nkhani