Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 9:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu.

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:1 nkhani