Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 2:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Koma anakhalapo ena a alembi akuganizira mumtima mwao,

7. Munthu amene atero bwanji? acita mwano; akhoza ndani kukhululukira macimo, koma mmodzi, ndiye Mulungu?

8. Ndipo pomwepo Yesu pozindikira mumtima mwace kuti alikuganizira comweco mwa iwo okha, ananena nao, Muganiza bwanji zinthu izi m'mitima yanu?

Werengani mutu wathunthu Marko 2