Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pomwepo Yesu pozindikira mumtima mwace kuti alikuganizira comweco mwa iwo okha, ananena nao, Muganiza bwanji zinthu izi m'mitima yanu?

Werengani mutu wathunthu Marko 2

Onani Marko 2:8 nkhani