Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 16:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaturuka iwo, nathawa kumanda; pakuti kunthunthumira ndi kudabwa kwakukuru kudawagwira; ndipo sanauza kanthu kwa munthu ali yense; pakuti anacitamantha.

Werengani mutu wathunthu Marko 16

Onani Marko 16:8 nkhani