Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 12:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Ndipo iwo anamtenga iye, nampanda, namcotsa wopanda kanthu.

4. Ndipo anatumanso kapolo wina kwa iwo; ndipo ameneyu anamlasa mutu, namcitira zomcititsa manyazi.

5. Ndipo anatuma wina; iyeyu anamupha; ndi ena ambiri; ena anawapanda, ndi ena anawapha.

6. Anamtsalira mmodzi, ndiye mwana wace wokondedwa; potsiriza anamtuma iye kwa iwo, nanena, Adzamcitira ulemu mwana wanga.

Werengani mutu wathunthu Marko 12