Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 12:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anamtsalira mmodzi, ndiye mwana wace wokondedwa; potsiriza anamtuma iye kwa iwo, nanena, Adzamcitira ulemu mwana wanga.

Werengani mutu wathunthu Marko 12

Onani Marko 12:6 nkhani