Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 9:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. pakuti Ine ndidzamuonetsa iye zinthu zambirl ayenera iye kuzimva kuwawa cifukwaca dzina langa.

17. Ndipo anacoka Hananiya, nalowa m'nyumbayo; ndipo anaika manja ace pa iye, nati, Saulo, mbale, Ambuye wandituma ine, ndiye Yesu amene anakuonekerani pa njira wadzerayo, kuti upenyenso, ndi kudzazidwa ndi Mzimu Woyera.

18. Ndipo pomwepo padagwa kucoka m'maso mwace ngati mamba, ndipo anapenyanso;

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 9