Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 26:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene tidagwa pansi tonse, ndinamva mau akunena kwa ine m'cinenedwe ca Cihebri, Saulo, Saulo, undilondalonderanji Ine? nkukubvuta kutsalima pacothwikira.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 26

Onani Macitidwe 26:14 nkhani