Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 21:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'mawa mwace tinacoka, ntinafika ku Kaisareya, ndipo m'mene tinalowa m'nyumba ya Filipo mlaliki, mmodzi wa asanu ndi awiri aja, tinakhala naye.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 21

Onani Macitidwe 21:8 nkhani