Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 21:23-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Cifukwa cace ucite ici tikuuza iwe; tiri nao amuna anai amene anawinda;

24. amenewa uwatenge nudziyeretse nao pamodzi, nuwalipirire, kati amete mutu; ndipo adzadziwa onse kuti zomveka za iwe nzacabe, koma kuti iwe wekhaoso uyenda molunjika, nusunga cilamulo.

25. Kama kunena za amitundu adakhulupirawo, tinalembera ndi kulamulira kuti asale zoperekedwa kwa mafano, ndi mwazi, ndi zopotola, ndi dama.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 21