Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 20:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo litaleka phokoso, Paulo anaitana ophunzirawo, ndipo m'mene anawacenjeza, analawirana nao, naturuka kunka ku Makedoniya.

2. Ndipo m'mene atapitapita m'mbali zijazo, nawacenjeza, anadza ku Helene.

3. Ndipo m'mene adakhalako miyezi itatu, ndipo a atampangira ciwembu Ayuda, pori iye apite ndi ngalawa ku Suriya, anatsimikiza mtima abwerere popyola Makedoniya.

4. Ndipo anamperekeza kufikira ku Asiya Sopatro mwana wa Puro, wa ku Bereya; ndipo Atesalonika, Aristarko ndi Sekundo; ndi Gayo wa ku Derbe, ndi Timoteo; ndi a ku Asiya, Tukiko ndi Trofimo.

5. Koma iwowa adatitsogolera, natilinda ku Trowa.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 20