Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 19:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene ena anaumitsa mtima ndi kusamvera, nanenera zoipa Njirayo pamaso pa anthu, anawacokera, napatutsa akuphunzira, nafotokozera masiku onse m'sukulu ya Turano.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 19

Onani Macitidwe 19:9 nkhani