Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 19:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye analowa m'sunagoge, nanena molimba mtima, miyezi itatu, natsutsana ndi kukopa kunena za Ufumu wa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 19

Onani Macitidwe 19:8 nkhani