Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 19:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo panali, pamene Apolo anali ku Korinto, Paulo anapita pa maiko a pamtunda, nafika ku Efeso, napeza akuphunzira ena;

2. ndipo anati kwa iwo, Kodi munalandira Mzimu Woyera pamene munakhulupira? Ndipo anati, lai, sitinamva konsekuti Mzimu Woyera waperekedwa.

3. Ndipo anati, Nanga mwabatizidwa m'ciani? Ndipo anai, Mu ubatizo wa Yohane.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 19