Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 17:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akukonda nzeru ena a Epikureya ndi a Stoiki anatengana naye. Ena anati, ici ciani afuna kunena wobwetuka uyu? Ndipo ena, Anga wolalikira ziwanda zacilendo, cifukwa analalikira Yesu ndi kuuka kwa akufa.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 17

Onani Macitidwe 17:18 nkhani