Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 13:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mulungu wa anthu awa Israyeli anasankha makolo athu, nakweza anthuwo pakugonerera iwo m'dziko la Aigupto, ndipo ndi dzanja lokwezeka anawaturutsa iwo m'menemo.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 13

Onani Macitidwe 13:17 nkhani