Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 12:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Petro atatsitsimuka, anati, Tsopano ndidziwa zoona, kuti Ambuye anatuma mngelo wace nandilanditsa ine m'dzanja la Herode, ndi ku cilingiriro conse ca anthu a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 12

Onani Macitidwe 12:11 nkhani