Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 11:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo iwotu, akubalalika cifukwa ca cisautsoco cidadza pa Stefano, anafikira ku Foinike, ndi Kupro, ndi Antiokeya, osalankhula mau kwa wina yense koma kwa Ayuda okha.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 11

Onani Macitidwe 11:19 nkhani